Malawi National Anthem
Mulungu dalitsa Malawi
God Bless Malawi
1964
1964
Michael-Fredrick Paul Sauka
Michael-Fredrick Paul Sauka
✝ God / Faith 🤝 Unity 🕊 Freedom 🌿 Nature ☮ Peace |
Key Facts
- 1. Michael-Fredrick Paul Sauka wrote both the lyrics and the music for the anthem
- 2. The anthem specifically asks God to defeat hunger, disease, and envy, reflecting the practical challenges facing the young nation at independence
- 3. Malawi is known as 'The Warm Heart of Africa' due to the friendliness of its people, a spirit reflected in the anthem's call for mutual love
Malawi National Anthem Lyrics
Mlungu dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogoleri nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.
Malaŵi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malaŵi.
O Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malaŵi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mayi, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malaŵi.
Translations are non-official and intended to convey meaning, not replace originals
Analysis
EditorialWritten and composed by Michael-Fredrick Paul Sauka, adopted upon independence from Britain in 1964. The anthem is a prayerful call for peace, unity, and freedom from hardship. It is sung in Chichewa, the most widely spoken language in Malawi.
Learn More
Sources & References
- Mlungu dalitsani Malaŵi . Wikipedia
Source & Review
- Source status
- Wikipedia source
- Translation
- AI-assisted working translation
- Rights status
- Third-party rights may apply
- Last reviewed
- Editorial review
- AI-assisted editorial review
- Editorial owner
- Nationalia
- Report a correction
- rights@nationalia.org