All anthems

Malawi National Anthem

Mulungu dalitsa Malawi

God Bless Malawi

1964
1964
Michael-Fredrick Paul Sauka
Michael-Fredrick Paul Sauka
God / Faith 🤝 Unity 🕊 Freedom 🌿 Nature Peace |

Key Facts

  • 1. Michael-Fredrick Paul Sauka wrote both the lyrics and the music for the anthem
  • 2. The anthem specifically asks God to defeat hunger, disease, and envy, reflecting the practical challenges facing the young nation at independence
  • 3. Malawi is known as 'The Warm Heart of Africa' due to the friendliness of its people, a spirit reflected in the anthem's call for mutual love
Malawi - Mulungu dalitsa Malawi

Malawi National Anthem Lyrics

Mlungu dalitsani Malaŵi, Mumsunge m'mtendere. Gonjetsani adani onse, Njala, nthenda, nsanje. Lunzitsani mitima yathu, Kuti tisaope. Mdalitse Mtsogoleri nafe, Ndi Mayi Malaŵi. Malaŵi ndziko lokongola, La chonde ndi ufulu, Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri, Ndithudi tadala. Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu, N'mphatso zaulere. Nkhalango, madambo abwino. Ngwokoma Malaŵi. O Ufulu tigwirizane, Kukweza Malaŵi. Ndi chikondi, khama, kumvera, Timutumikire. Pa nkhondo nkana pa mtendere, Cholinga n'chimodzi. Mayi, bambo, tidzipereke, Pokweza Malaŵi.

Translations are non-official and intended to convey meaning, not replace originals

Analysis

Editorial

Written and composed by Michael-Fredrick Paul Sauka, adopted upon independence from Britain in 1964. The anthem is a prayerful call for peace, unity, and freedom from hardship. It is sung in Chichewa, the most widely spoken language in Malawi.

Learn More

Sources & References

  1. Mlungu dalitsani Malaŵi . Wikipedia

Source & Review

Source status
Wikipedia source
Translation
AI-assisted working translation
Rights status
Third-party rights may apply
Last reviewed
Editorial review
AI-assisted editorial review
Editorial owner
Nationalia
Report a correction
rights@nationalia.org

Related anthems